Luka 2:35 - Buku Lopatulika35 eya, ndipo lupanga lidzakupyoza iwe moyo wako; kuti maganizo a m'mitima yambiri akaululidwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 eya, ndipo lupanga lidzakupyoza iwe moyo wako; kuti maganizo a m'mitima yambiri akaululidwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 kuti choncho maganizo amene ali m'mitima ya anthu ambiri adzaonekere poyera. Ndipo inunso mai, chisoni chidzabaya mtima wanu ngati lupanga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 kotero kuti malingaliro a mitima ya ambiri adzawululidwa. Ndipo lupanga lidzabaya moyo wakonso.” Onani mutuwo |