Luka 19:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo anafika woyamba, nanena, Mbuye, mina yanu inachita nionjeza mina khumi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo anafika woyamba, nanena, Mbuye, mina yanu inachita nionjeza mina khumi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Woyamba adadza nati, ‘Ambuye, ndalama yanu ija idapindula ndalama makumi khumi.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 “Woyamba anabwera ndipo anati, ‘Bwana ndalama zanu zapindula khumi zina.’ Onani mutuwo |