Luka 19:12 - Buku Lopatulika12 Pamenepo anati, Munthu wa fuko lomveka ananka kudziko lakutali, kudzilandirira yekha ufumu, ndi kubwerako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Pamenepo anati, Munthu wa fuko lomveka ananka kudziko lakutali, kudzilandirira yekha ufumu, ndi kubwerako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Adati, “Munthu wina, wa fuko lomveka, adapita ku dziko lakutali kukalandira ufumu kuti pambuyo pake abwerenso kwao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Iye anati, “Munthu wa banja laufumu anapita ku dziko lakutali kukadzozedwa ufumu ndipo kenaka abwerenso kwawo. Onani mutuwo |