Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 18:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo Ambuye anati, Tamverani chonena woweruza wosalungama.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo Ambuye anati, Tamverani chonena woweruza wosalungama.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Tsono Ambuye adati, “Mwamvatu mau a woweruza wosalungama uja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Ndipo Ambuye anati, “Tamvani zimene woweruza wopanda chilungamoyu wanena.

Onani mutuwo Koperani




Luka 18:6
4 Mawu Ofanana  

kotero kuti mukakhale ana a Atate wanu wa Kumwamba; chifukwa Iye amakwezera dzuwa lake pa oipa ndi pa abwino, namavumbitsira mvula pa olungama ndi pa osalungama.


Ndipo pamene Ambuye anamuona, anagwidwa ndi chifundo chifukwa cha iye, nanena naye, Usalire.


Ndipo Yohane anaitana awiri a ophunzira ake, nawatuma kwa Ambuye, nanena, Kodi ndinu wakudzayo, kapena tiyang'anire wina?


kodi simunasiyanitse mwa inu nokha, ndi kukhala oweruza oganizira zoipa?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa