Luka 17:3 - Buku Lopatulika3 Kadzichenjerani nokha; akachimwa mbale wako umdzudzule, akalapa, umkhululukire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Kadzichenjerani nokha; akachimwa mbale wako umdzudzule, akalapa, umkhululukire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Chenjerani tsono! “Mbale wako akachimwa, umdzudzule. Akatembenuka mtima, umkhululukire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Nʼchifukwa chake dziyangʼanireni nokha. “Ngati mʼbale wanu achimwa, mudzudzuleni, ndipo ngati alapa, mukhululukireni. Onani mutuwo |