Luka 16:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo m'dziko la akufa anakweza maso ake, pokhala nao mazunzo, naona Abrahamu patali, ndi Lazaro m'chifuwa mwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo m'dziko la akufa anakweza maso ake, pokhala nao mazunzo, naona Abrahamu patali, ndi Lazaro m'chifuwa mwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Pamene ankazunzika ku Malo a anthu akufa, wachuma uja adayang'ana kumwamba naona Abrahamu ali patali, ndi Lazaro ali pambali pakepa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Ali mʼgehena kuzunzika, anakweza maso ake ndipo anaona Abrahamu ali ndi Lazaro pambali pake. Onani mutuwo |