Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 15:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo m'mene aipeza amema abwenzi ake ndi anansi ake, nanena, Kondwerani ndi ine, chifukwa ndinapeza ndalama ndidatayayo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo m'mene aipeza amema abwenzi ake ndi anansi ake, nanena, Kondwerani ndi ine, chifukwa ndinapeza ndalama ndidatayayo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Atakapeza amasonkhanitsa abwenzi ake ndi anzake oyandikana nawo, naŵauza kuti, ‘Mukondwere nane pamodzi, chifukwa ndakapeza kandalama kanga kaja kadaatayikaka.’ ”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Ndipo pamene wayipeza, amayitana anzake, ndi anansi pamodzi nati, ‘Kondwerani nane; ine ndayipeza ndalama yanga yotayika ija.’

Onani mutuwo Koperani




Luka 15:9
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anansi ake ndi abale ake anamva kuti Ambuye anakulitsa chifundo chake pa iye; nakondwera naye pamodzi.


Chomwecho, ndinena kwa inu, kuli chimwemwe pamaso pa angelo a Mulungu chifukwa cha munthu wochimwa mmodzi amene atembenuka mtima.


Kapena mkazi wanji ali nazo ndalama zasiliva khumi, ngati itayika imodzi, sayatsa nyali, nasesa m'nyumba yake, nafunafuna chisamalire kufikira akaipeza?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa