Luka 15:19 - Buku Lopatulika19 sindiyeneranso konse kutchulidwa mwana wanu; mundiyese ine ngati mmodzi wa antchito anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 sindiyeneranso konse kutchulidwa mwana wanu; mundiyese ine ngati mmodzi wa antchito anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Sindili woyenera kutchedwanso mwana wanu. Mundilole ndisanduke mmodzi mwa antchito anu.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Ndine wosayeneranso kutchedwa mwana wanu; munditenge ngati mmodzi wa antchito anu.’ Onani mutuwo |