Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 15:11 - Buku Lopatulika

11 Ndipo Iye anati, Munthu wina anali ndi ana aamuna awiri;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo Iye anati, Munthu wina anali ndi ana amuna awiri;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Yesu adatinso, “Munthu wina adaali ndi ana aamuna aŵiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Yesu anapitiriza kunena kuti, “Panali munthu amene anali ndi ana aamuna awiri.

Onani mutuwo Koperani




Luka 15:11
4 Mawu Ofanana  

Pakuti monga ana a Yonadabu mwana wa Rekabu achita lamulo la kholo lao limene anawauza, koma anthu awa sanandimvere Ine.


Chomwecho, ndinena kwa inu, kuli chimwemwe pamaso pa angelo a Mulungu chifukwa cha munthu wochimwa mmodzi amene atembenuka mtima.


ndipo wamng'onoyo anati kwa atate wake, Atate, ndigawirenitu zanga za pa chuma chanu. Ndipo iye anawagawira za moyo wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa