Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 14:34 - Buku Lopatulika

34 Kotero mchere uli wokoma; koma ngati mchere utasukuluka adzaukoleretsa ndi chiyani?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 Kotero mchere uli wokoma; koma ngati mchere utasukuluka adzaukoleretsa ndi chiyani?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 “Mchere ndi wabwino. Koma ngati mcherewo watha mphamvu, mphamvu zakezo nkuzibwezeranso nchiyani?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 “Mchere ndi wabwino, koma ngati usukuluka adzawukoleretsanso ndi chiyani?

Onani mutuwo Koperani




Luka 14:34
4 Mawu Ofanana  

Inu ndinu mchere wa dziko lapansi; koma mcherewo ngati ukasukuluka, adzaukoleretsa ndi chiyani? Pamenepo sungakwanirenso kanthu konse, koma kuti ukaponyedwe kunja, nupondedwe ndi anthu.


Mau anu akhale m'chisomo, okoleretsa, kuti mukadziwe inu mayankhidwe anu a kwa yense akatani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa