Luka 14:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo panali pamene Iye analowa m'nyumba ya mmodzi wa akulu a Afarisi tsiku la Sabata, kukadya, iwo analikumzonda Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo panali pamene Iye analowa m'nyumba ya mmodzi wa akulu a Afarisi tsiku la Sabata, kukadya, iwo analikumzonda Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pa tsiku lina la Sabata Yesu adakadya kwa mkulu wina wa m'gulu la Afarisi, ndipo Afarisi anzake ankamupenyetsetsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Pa tsiku lina la Sabata, Yesu atapita kukadya ku nyumba ya Mfarisi wodziwika, Afarisi anamulonda mosamalitsa. Onani mutuwo |