Luka 13:18 - Buku Lopatulika18 Pamenepo ananena, Ufumu wa Mulungu ufanana ndi chiyani? Ndipo ndidzaufanizira ndi chiyani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Pamenepo ananena, Ufumu wa Mulungu ufanana ndi chiyani? Ndipo ndidzaufanizira ndi chiyani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Yesu adati, “Kodi Ufumu wa Mulungu uli ngati chiyani, ndipo ndingauyerekeze ndi chiyani? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Kenaka Yesu anafunsa kuti, “Kodi ufumu wa Mulungu uli ngati chiyani? Kodi Ine ndingawufanizire ndi chiyani? Onani mutuwo |