Luka 12:44 - Buku Lopatulika44 Ndinena ndinu zoona, kuti adzamuika iye kapitao wa pa zonse ali nazo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201444 Ndinena ndinu zoona, kuti adzamuika iye kapitao wa pa zonse ali nazo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa44 Ndithu ndikunenetsa kuti adzamuika woyang'anira chuma chake chonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero44 Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti adzamuyika kukhala woyangʼanira katundu wake yense. Onani mutuwo |