Luka 11:40 - Buku Lopatulika40 Opusa inu, kodi Iye wopanga kunja kwake sanapangenso m'kati mwake? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Opusa inu, kodi Iye wopanga kunja kwake sanapangenso m'kati mwake? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Ndinu anthu opusa! Kodi Mulungu amene adapanga zakunja, si yemweyo adapanganso zam'kati? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Anthu opusa inu! Kodi amene anapanga zamʼkati sanapangenso zakunja? Onani mutuwo |