Luka 11:30 - Buku Lopatulika30 Pakuti monga ngati Yona anali chizindikiro kwa Aninive, chotero adzakhalanso Mwana wa Munthu kwa mbadwo uno. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Pakuti monga ngati Yona anali chizindikiro kwa Aninive, chotero adzakhalanso Mwana wa Munthu kwa mbadwo uno. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Monga Yona uja anali chizindikiro kwa anthu a ku Ninive, chomwechonso Mwana wa Munthu adzakhala chizindikiro kwa anthu a mbadwo uno. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Monga Yona uja anali chizindikiro kwa anthu ku Ninive, momwemonso Mwana wa Munthu adzakhala chizindikiro kwa anthu a mʼbado uno. Onani mutuwo |