Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 11:25 - Buku Lopatulika

25 ndipo pofika, uipeza yosesa ndi yokonzeka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 ndipo pofika, uipeza yosesa ndi yokonzeka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Tsono ukafika, umapeza m'nyumba muja muli mosesasesa ndi mokonza bwino.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Ukafika umapeza mʼnyumba mosesedwa bwino ndi mokonza.

Onani mutuwo Koperani




Luka 11:25
10 Mawu Ofanana  

Koma iwo akupatula kutsata njira zao zokhotakhota, Yehova adzawachotsa pamodzi ndi ochita zopanda pake. Mtendere ukhale pa Israele.


Mau a pakamwa pake ndiwo opanda pake ndi onyenga, waleka kuzindikira ndi kuchita bwino.


Pamene paliponse mzimu wonyansa ukatuluka mwa munthu, upyola malo opanda madzi nufunafuna mpumulo; ndipo posaupeza unena, Ndidzabwera kunyumba kwanga kumene ndinatulukako;


Pomwepo upita nutenga mizimu ina isanu ndi iwiri yoipa yoposa ndi uwu mwini; ndipo ilowa nikhalira komweko; ndipo makhalidwe otsiriza a munthu uyu aipa koposa oyambawo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa