Luka 10:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo anati kwa iye, M'chilamulo mulembedwa chiyani? Uwerenga bwanji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo anati kwa iye, M'chilamulo mulembedwa chiyani? Uwerenga bwanji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Yesu adati, “Kodi m'Malamulo mudalembedwa chiyani? Mumaŵerengamo zotani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Yesu anayankha kuti, “Mwalembedwa chiyani mʼMalamulo, ndipo iwe umawerenga zotani?” Onani mutuwo |