Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 10:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo m'mene anapotolokera kwa ophunzira ake, ali pa okha, anati, Odala masowo akuona zimene muona.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo m'mene anapotolokera kwa ophunzira ake, ali pa okha, anati, Odala masowo akuona zimene muona.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Pambuyo pake Yesu adatembenukira ophunzira ake, naŵauza iwo okha kuti, “Ngodala maso amene akuwona zimene mukuwonazi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Kenaka anatembenukira kwa ophunzira ake nawawuza iwo okha kuti, “Ndi odala maso amene akuona zimene mukuonazi.

Onani mutuwo Koperani




Luka 10:23
2 Mawu Ofanana  

Pakuti ndinena ndi inu kuti aneneri ndi mafumu ambiri anafuna kuona zimene inu muziona, koma sanazione; ndi kumva zimene mukumva, koma sanazimve.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa