Luka 10:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo anati kwa iwo, Ndinaona Satana alinkugwa ngati mphezi wochokera kumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo anati kwa iwo, Ndinaona Satana alinkugwa ngati mphezi wochokera kumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Yesu adaŵauza kuti, “Ndidaona Satana alikugwa ngati mphezi kuchokera Kumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Iye anayankha kuti, “Ndinaona Satana akugwa kuchokera kumwamba ngati mphenzi. Onani mutuwo |