Luka 1:65 - Buku Lopatulika65 Ndipo panagwa mantha pa iwo onse akukhala oyandikana nao; ndipo analankhulalankhula nkhani izi zonse m'dziko lonse la mapiri a Yudeya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201465 Ndipo panagwa mantha pa iwo onse akukhala oyandikana nao; ndipo analankhulalankhula nkhani izi zonse m'dziko lonse la mapiri a Yudeya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa65 Anzao onse aja adagwidwa ndi mantha, ndipo mbiri ya zimenezi idawanda ku dera lonse la mapiri a ku Yudeya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero65 Anansi onse anachita mantha kwambiri, ndipo ku madera onse a kumapiri a Yudeya, anthu anayankhula zinthu zonsezi. Onani mutuwo |