Luka 1:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo udzakhala nako kukondwera ndi msangalalo; ndipo anthu ambiri adzakondwera pa kubadwa kwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo udzakhala nako kukondwera ndi msangalalo; ndipo anthu ambiri adzakondwera pa kubadwa kwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 “Udzakondwa ndi kusangalala, anthu ambirinso adzakondwa chifukwa cha kubadwa kwake, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ndipo adzakhala chimwemwe ndi chisangalalo kwa iwe, ndipo ambiri adzasangalala chifukwa cha kubadwa kwake, Onani mutuwo |