Levitiko 24:2 - Buku Lopatulika2 Uza ana a Israele, kuti akutengere mafuta a azitona oyera opera akuunikira, kuti aziwalitsa nyali nthawi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Uza ana a Israele, kuti akutengere mafuta a azitona oyera opera akuunikira, kuti aziwalitsa nyali nthawi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Lamula Aisraele kuti akupatse mafuta anyale, a olivi wabwino kwambiri, kuti nyale izikhala yoyaka nthaŵi zonse m'Nyumba mwanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Lamula Aisraeli kuti akupatse mafuta anyale, a olivi wabwino kwambiri kuti nyalezo ziziyaka nthawi zonse. Onani mutuwo |