Levitiko 17:9 - Buku Lopatulika9 osadza nayo ku khomo la chihema chokomanako, kuiphera Yehova; amsadze munthuyu kumchotsa kwa anthu a mtundu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 osadza nayo ku khomo la chihema chokomanako, kuiphera Yehova; amsadze munthuyu kumchotsa kwa anthu a mtundu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 akapanda kubwera nayo pakhomo pa chihema chamsonkhano kudzaipereka pamaso pa Chauta, munthu ameneyo achotsedwe pakati pa anthu anzake.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 popanda kubwera nayo pa khomo la tenti ya msonkhano kudzayipereka pamaso pa Yehova, munthu ameneyo achotsedwe pakati pa anthu anzake.’ ” Onani mutuwo |