Levitiko 17:3 - Buku Lopatulika3 Munthu aliyense wa mbumba ya Israele akapha ng'ombe, kapena mwanawankhosa, kapena mbuzi, m'chigono, kapena akaipha kunja kwa chigono, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Munthu aliyense wa mbumba ya Israele akapha ng'ombe, kapena mwanawankhosa, kapena mbuzi, m'chigono, kapena akaipha kunja kwa chigono, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 ‘Mwisraele aliyense akapha ng'ombe, kapena mwanawankhosa, kapena mbuzi, ku zithando kapena kunja kwa zithando, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mwisraeli aliyense amene apha ngʼombe, mwana wankhosa kapena mbuzi mu msasa kapena kunja kwa msasa, Onani mutuwo |