Levitiko 17:2 - Buku Lopatulika2 Nena ndi Aroni, ndi ana ake aamuna, ndi ana a Israele onse, nuti nao, Ichi ndi chimene Yehova wauza, ndi kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Nena ndi Aroni, ndi ana ake amuna, ndi ana a Israele onse, nuti nao, Ichi ndi chimene Yehova wauza, ndi kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Uza Aroni ndi ana ake, pamodzi ndi Aisraele onse, kuti Chauta akulamula kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Uza Aaroni ndi ana ake, pamodzi ndi Aisraeli onse kuti, ‘Chimene Yehova walamula ndi ichi: Onani mutuwo |