Hoseya 2:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo kudzachitika tsiku lomwelo, ndidzavomereza, ati Yehova, ndidzavomereza thambo, ndi ilo lidzavomereza dziko lapansi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo kudzachitika tsiku lomwelo, ndidzavomereza, ati Yehova, ndidzavomereza thambo, ndi ilo lidzavomereza dziko lapansi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Chauta akunena kuti, “Nthaŵi imeneyo ndidzamvera mlengalenga, mvula idzagwa pa dziko lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 “Tsiku limenelo Ine ndidzayankha,” akutero Yehova. “Ndidzayankha mlengalenga pempho lake lofuna mitambo ndipo mvula idzagwa pa dziko lapansi; Onani mutuwo |