Hoseya 2:1 - Buku Lopatulika1 Nenani kwa abale anu, Anthu anga, ndi kwa alongo anu, Wochitidwa-chifundo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Nenani kwa abale anu, Anthu anga, ndi kwa alongo anu, Wochitidwa-chifundo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Nchifukwa chake abale ako uŵauze kuti, “Ndinu anthu a Chauta”, ndiponso kuti, “Chauta wakukondani”. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 “Nena kwa abale ako kuti, ‘Ndinu anthu anga,’ kwa alongo ako kuti ‘Ndinu okondedwa anga.’ ” Onani mutuwo |