Hoseya 12:7 - Buku Lopatulika7 Ndiye Mkanani, m'dzanja lake muli miyeso yonyenga, akonda kusautsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndiye Mkanani, m'dzanja lake muli miyeso yonyenga, akonda kusautsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Chauta akuti, “Aisraele ali ngati wamalonda wonyenga amene amagwiritsa ntchito masikelo onama. Amakonda kumeta anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Munthu wamalonda amagwiritsa ntchito masikelo achinyengo; iyeyo amakonda kubera anthu. Onani mutuwo |
Ndikalipo ine; chitani umboni wonditsutsa pamaso pa Yehova, ndi pamaso pa wodzozedwa wake; ndinalanda ng'ombe ya yani? Kapena ndinalanda bulu wa yani? Ndinanyenga yani? Ndinasutsa yani? Ndinalandira m'manja mwa yani chokometsera mlandu kutseka nacho maso anga? Ngati ndinatero ndidzachibwezera kwa inu.