Hoseya 1:8 - Buku Lopatulika8 Ataleka tsono kuyamwitsa Wosachitidwa-chifundo, anaima, nabala mwana wamwamuna. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ataleka tsono kuyamwitsa Wosachitidwa-chifundo, anaima, nabala mwana wamwamuna. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Sakondedwa ataleka kuyamwa, Gomeri adatenganso pena pathupi, nabala mwana winanso wamwamuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Sakondedwa ataleka kuyamwa, Gomeri anabereka mwana wina wamwamuna. Onani mutuwo |