Hoseya 1:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo anamuka natenga Gomeri mwana wamkazi wa Dibulaimu; iye naima, nambalira mwana wamwamuna. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo anamuka natenga Gomeri mwana wamkazi wa Dibulaimu; iye naima, nambalira mwana wamwamuna. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Motero Hoseya adapita, nakakwatira mkazi, dzina lake Gomeri, mwana wa Dibulaimu. Mkaziyo adatenga pathupi, namubalira mwana wamwamuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Motero Hoseya anakwatira Gomeri mwana wamkazi wa Dibulaimu, ndipo mkaziyo anakhala woyembekezera nabala mwana wamwamuna. Onani mutuwo |