Genesis 8:16 - Buku Lopatulika16 Tulukamoni m'chingalawamo, iwe ndi ana ako, ndi mkazi wako, ndi akazi a ana ako pamodzi ndi iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Tulukamoni m'chingalawamo, iwe ndi ana ako, ndi mkazi wako, ndi akazi a ana ako pamodzi ndi iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 “Iwe ndi mkazi wako, ana ako pamodzi ndi akazi ao, tulukani m'chombomo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 “Iwe, mkazi wako, ana ako pamodzi ndi akazi awo tulukani mʼchombomo. Onani mutuwo |