Genesis 50:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo Yosefe analumbiritsa ana a Israele kuti, Mulungu adzaonekera kwa inu ndithu, ndipo mudzakwera nao mafupa anga kuchokera kuno. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo Yosefe analumbiritsa ana a Israele kuti, Mulungu adzaonekera kwa inu ndithu, ndipo mudzakwera nao mafupa anga kuchokera kuno. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Kenaka Yosefe adapempha ana a Israele kuti alumbire. Adati, “Lonjezeni kuti Mulungu akakusungani, mudzasenza mafupa anga kuchoka nawo kuno.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Ndipo Yosefe analumbiritsa ana a Israeli lumbiro nati, “Lonjezani kuti Mulungu akadzakusungani mudzanyamula mafupa anga kuwachotsa ku malo kuno.” Onani mutuwo |