Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 5:28 - Buku Lopatulika

28 Ndipo Lameki anakhala ndi moyo zaka zana kudza makumi asanu ndi atatu ndi ziwiri, nabala mwana wamwamuna;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Ndipo Lameki anakhala ndi moyo zaka zana kudza makumi asanu ndi atatu ndi ziwiri, nabala mwana wamwamuna;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Lameki ali wa zaka 182, adabereka mwana,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Pamene Lameki anali ndi zaka 182, anabereka mwana wamwamuna.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 5:28
3 Mawu Ofanana  

masiku ake onse a Metusela anali mazana asanu ndi anai kudza makumi asanu ndi limodzi kudza zisanu ndi zinai; ndipo anamwalira.


namutcha dzina lake Nowa, ndi kuti, Yemweyu adzatonthoza mtima wathu pantchito zathu zovuta za manja athu, chifukwa cha nthaka imene anaitemberera Yehova;


mwana wa Kainani, mwana wa Arifaksadi, mwana wa Semu, mwana wa Nowa, mwana wa Lameki,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa