Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 5:26 - Buku Lopatulika

26 ndipo Metusela anakhala ndi moyo, atabala Lameki, zaka mazana asanu ndi awiri kudza makumi asanu ndi atatu ndi ziwiri, nabala ana aamuna ndi aakazi:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 ndipo Metusela anakhala ndi moyo, atabala Lameki, zaka mazana asanu ndi awiri kudza makumi asanu ndi atatu ndi awiri, nabala ana aamuna ndi aakazi:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 ndipo adakhalanso ndi moyo zaka zina 782. Adaberekanso ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Ndipo atabadwa Lameki, Metusela anakhala ndi moyo zaka zina 782 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 5:26
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Metusela anakhala ndi moyo zaka zana kudza makumi asanu ndi atatu ndi zisanu ndi ziwiri, nabala Lameki;


masiku ake onse a Metusela anali mazana asanu ndi anai kudza makumi asanu ndi limodzi kudza zisanu ndi zinai; ndipo anamwalira.


Masiku ake Adamu atabala Seti, anali zaka mazana asanu ndi atatu; ndipo anabala ana aamuna ndi aakazi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa