Genesis 48:4 - Buku Lopatulika4 Taona, ndidzakubalitsa iwe, ndidzakuchulukitsa iwe, ndidzakusandutsa iwe khamu la anthu a mitundu; ndipo ndidzapatsa mbeu yako ya pambuyo pako dziko ili likhale laolao chikhalire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Taona, ndidzakubalitsa iwe, ndidzakuchulukitsa iwe, ndidzakusandutsa iwe khamu la anthu a mitundu; ndipo ndidzapatsa mbeu yako ya pambuyo pako dziko ili likhale laolao chikhalire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Adandiwuza kuti, ‘Ndidzakupatsa ana ambiri kotero kuti zidzukulu zako zidzasanduka mitundu yambiri ya anthu. Dziko lino ndidzapatsa zidzukulu zako kuti likhale lao mpaka muyaya.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 nati kwa ine, ‘Ndidzakupatsa ana ambiri ndipo zidzukulu zako zidzasanduka mitundu yambiri ya anthu. Ndidzapereka dziko ili kwa zidzukulu zako zobwera pambuyo pako kuti likhale lawo mpaka muyaya.’ Onani mutuwo |