Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 47:21 - Buku Lopatulika

21 Tsono anthu, anasunthira iwo kumizinda kuchokera kumphepete kwa malire a Ejipito kufikira kumphepete kwina kwake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Tsono anthu, anasunthira iwo kumidzi kuchokera kumphepete kwa malire a Ejipito kufikira kumphepete kwina kwake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Yosefe adaŵasandutsa akapolo anthuwo ponseponse m'dziko la Ejipito.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 ndipo Yosefe anawasandutsa anthu onse kukhala akapolo a Farao, kuchokera ku malire a mbali ina ya Igupto kukafika ku malire a mbali ina ya dzikolo.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 47:21
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anasonkhanitsa chakudya chonse cha zaka zisanu ndi ziwiri chimene chinali m'dziko la Ejipito, nasunga chakudyacho m'mizinda; chakudya cha m'minda, yozinga mizinda yonse, anachisunga m'menemo.


Ndipo Yosefe anamgulira Farao dziko lonse la Ejipito, chifukwa Aejipito anagulitsa yense munda wake, chifukwa njala inakula pa iwo; ndipo dziko linakhala la Farao.


Koma dziko la ansembe lokha sanagule, chifukwa ansembe analandira gawo lao kwa Farao, nadya gawolo anawapatsa Farao; chifukwa chake sanagulitse dziko lao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa