Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 47:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo mwa abale ake anatengako anthu asanu, nawaonetsa iwo kwa Farao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo mwa abale ake anatengako anthu asanu, nawaonetsa iwo kwa Farao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Aŵa ndi asanu mwa abale angawo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Iye anapita kwa Farao kuja ndi abale ake asanu, kukawaonetsa.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 47:2
5 Mawu Ofanana  

Ndipo padzakhala pamene Farao adzaitana inu, nadzati, Ntchito yanu njotani?


Ndipo pa ulendo wachiwiri Yosefe anazindikirika ndi abale ake; ndipo fuko la Yosefe linaonekera kwa Farao.


podziwa kuti Iye amene anaukitsa Ambuye Yesu adzaukitsa ifenso pamodzi ndi Yesu, nadzatiikapo pamodzi ndi inu.


amene timlalikira ife, ndi kuchenjeza munthu aliyense ndi kuphunzitsa munthu aliyense mu nzeru zonse, kuti tionetsere munthu aliyense wamphumphu mwa Khristu;


Ndipo kwa Iye amene akhoza kukudikirani mungakhumudwe, ndi kukuimikani pamaso pa ulemerero wake opanda chilema m'kukondwera,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa