Genesis 43:10 - Buku Lopatulika10 pakuti tikadaleka kuchedwa mwenzi tsopano titabwera kawiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 pakuti tikadaleka kuchedwa mwenzi tsopano titabwera kawiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Tikadapanda kuzengereza, tikadapita ndi kubwerako kaŵiri konse tsopano.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Mmene zililimu, tikanapanda kuchedwa, bwenzi titapita ndi kubwerako kawiri.” Onani mutuwo |