Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 43:10 - Buku Lopatulika

10 pakuti tikadaleka kuchedwa mwenzi tsopano titabwera kawiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 pakuti tikadaleka kuchedwa mwenzi tsopano titabwera kawiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Tikadapanda kuzengereza, tikadapita ndi kubwerako kaŵiri konse tsopano.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Mmene zililimu, tikanapanda kuchedwa, bwenzi titapita ndi kubwerako kawiri.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 43:10
3 Mawu Ofanana  

Koma anachedwa; ndipo anthuwo anamgwira dzanja lake, ndi dzanja la mkazi wake ndi dzanja la ana ake aakazi awiri; chifukwa cha kumchitira chifundo Yehova; ndipo anamtulutsa iye, namuika kunja kwa mzinda.


Ndipo Israele atate wao anati kwa iwo, Ngati chomwecho tsopano chitani ichi: tengani zipatso za m'dziko muno m'zotengera zanu, mumtengere munthu uja mphatso, mafuta amankhwala pang'ono, ndi uchi pang'ono, zonunkhira ndi mure, ndi mfula, ndi katungurume;


Ine ndidzakhala chikole, pa manja anga mudzamfunsa: ndikapanda kumbwezera kwa inu ndi kumuimitsa pamaso panu, chifukwa chake chidzakhala pa ine masiku onse:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa