Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 42:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo Yosefe anazindikira abale ake, koma iwo sanamzindikire iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo Yosefe anazindikira abale ake, koma iwo sanamzindikire iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Yosefe adaŵazindikira abale ake aja, koma iwo sadamzindikire.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Ngakhale Yosefe anawazindikira abale ake, koma iwo sanamuzindikire.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 42:8
5 Mawu Ofanana  

Mibadwo ya Yakobo ndi iyi; Yosefe anali wa zaka khumi ndi zisanu ndi ziwiri analinkudyetsa zoweta pamodzi ndi abale ake; ndipo anali mnyamata pamodzi ndi ana a Biliha, ndi ana aamuna a Zilipa, akazi a atate wake; ndipo Yosefe anamfotokozera atate wake mbiri yao yoipa.


Ndipo Yosefe anali wa zaka makumi atatu pamene iye anaima pamaso pa Farao mfumu ya Aejipito. Ndipo Yosefe anatuluka pamaso pa Farao, napitapita padziko lonse la Ejipito.


Koma maso ao anagwidwa kuti asamzindikire Iye.


M'mene adanena izi, anacheuka m'mbuyo, naona Yesu ali chilili, ndipo sanadziwe kuti ndiye Yesu.


Koma pakuyamba kucha, Yesu anaimirira pambali pa nyanja, komatu ophunzirawo sanadziwe kuti ndiye Yesu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa