Genesis 4:8 - Buku Lopatulika8 Kaini ndipo ananena ndi Abele mphwake. Ndipo panali pamene anali kumunda, Kaini anamuukira Abele mphwake, namupha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Kaini ndipo ananena ndi Abele mphwake. Ndipo panali pamene anali kumunda, Kaini anamuukira Abele mphwake, namupha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Tsiku lina Kaini adauza mng'ono wake Abele kuti, “Tiye tikayende.” Atangopita kwa okha, Kaini adaukira mng'ono wakeyo namupha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Tsiku lina Kaini anati kwa mʼbale wake Abele, “Tiye tipite ku munda.” Ndipo ali ku mundako, Kaini anawukira mʼbale wake namupha. Onani mutuwo |