Genesis 4:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo Kaini anatuluka pamaso pa Yehova, ndipo anakhala m'dziko la Nodi, kum'mawa kwake kwa Edeni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo Kaini anatuluka pamaso pa Yehova, ndipo anakhala m'dziko la Nodi, kum'mawa kwake kwa Edeni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Tsono Kaini adachoka pamaso pa Chauta nakakhala m'dziko lotchedwa Nodi, kuvuma kwa Edeni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ndipo Kaini anachoka pamaso pa Yehova nakakhala ku dziko la Nodi, kummawa kwa Edeni. Onani mutuwo |