Genesis 36:34 - Buku Lopatulika34 Ndipo Yobabu anamwalira, ndipo Husamu wa ku dziko la Atemani analamulira m'malo mwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Ndipo Yobabu anamwalira, ndipo Husamu wa ku dziko la Atemani analamulira m'malo mwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Yobabu atafa, Husamu wa ku dziko la Atemani adaloŵa ufumu m'malo mwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Atafa Yobabu, Husamu wochokera ku dziko la Atemani, analowa mʼmalo mwake ngati mfumu. Onani mutuwo |