Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 34:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo Hamori atate wake wa Sekemu anatuluka kunka kwa Yakobo kukanena ndi iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo Hamori atate wake wa Sekemu anatuluka kunka kwa Yakobo kukanena ndi iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Hamori, bambo wa Sekemu, adapita kukacheza ndi Yakobe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Kenaka Hamori, abambo a Sekemu, anapita kukakambirana ndi Yakobo.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 34:6
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anamva Yakobo kuti anamuipitsa Dina, mwana wake wamkazi; ana ake aamuna anali ndi zoweta zake kudambo: ndipo Yakobo anakhala chete mpaka anafika iwo.


Ndipo pakumva icho ana ake aamuna a Yakobo anabwera pochokera kudambo: amunawo ndipo anapwetekwa mtima, nakwiya kwambiri, chifukwa iyeyo anachita chopusa choipira Israele pakugona ndi mwana wamkazi wa Yakobo; ndicho chosayenera kuchita.


Pamenepo Gaala, mwana wa Ebedi anati, Abimeleki ndani, ndi Sekemu ndani, kuti timtumikire? Sindiye mwana wa Yerubaala kodi? Ndi Zebuli kazembe wake? Mutumikire amuna a Hamori atate wa Sekemu; koma ameneyo timtumikire chifukwa ninji?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa