Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 32:8 - Buku Lopatulika

8 ndipo anati, Akafika Esau pa khamu limodzi nalikantha, linalo lotsala lidzapulumuka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 ndipo anati, Akafika Esau pa khamu limodzi nalikantha, linalo lotsala lidzapulumuka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Mumtima mwake ankaganiza kuti, “Esau akabwera, ndipo akachita nkhondo ndi gulu loyambali, gulu linalo lingathe kuthaŵa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Mʼmaganizo ake iye ankanena kuti, “Ngati Esau atabwera ndi kuthira nkhondo gulu limodzi, gulu lina lotsalalo likhoza kupulumuka.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 32:8
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Yakobo anaopa kwambiri, navutidwa; ndipo anagawa anthu anali nao ndi nkhosa ndi zoweta, ndi ngamira, zikhale makamu awiri;


Ndipo Yakobo anati, Mulungu wa atate wanga Abrahamu, Mulungu wa atate wanga Isaki, Yehova, amene munati kwa ine, Bwera ku dziko lako, ndi kwa abale ako, ndipo ndidzakuchitira iwe bwino:


Taonani, Ine ndikutumizani inu monga nkhosa pakati pa mimbulu; chifukwa chake khalani ochenjera monga njoka, ndi oona mtima monga nkhunda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa