Genesis 3:23 - Buku Lopatulika23 Yehova Mulungu anamtulutsa iye m'munda wa Edeni, kuti alime nthaka m'mene anamtenga iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Yehova Mulungu anamtulutsa iye m'munda wa Edeni, kuti alime nthaka m'mene anamtenga iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Motero Chauta adamtulutsamo m'munda mwa Edeni muja, kuti azilima m'nthaka momwe adachokera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Kotero Yehova Mulungu anatulutsa Adamu Mʼmunda wa Edeni kuti azilima mʼnthaka imene anachokera. Onani mutuwo |