Genesis 28:21 - Buku Lopatulika21 kuti ndibwerenso kunyumba ya atate wanga ndi mtendere, pamenepo Yehova adzakhala Mulungu wanga, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 kuti ndibwerenso kunyumba ya atate wanga ndi mtendere, pamenepo Yehova adzakhala Mulungu wanga, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 ndi kundibwezera bwino kwathu kwa atate anga, mudzakhala Mulungu wanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 ngati inu mudzandibweretsa kwathu mu mtendere, ndiye kuti mudzakhala Mulungu wanga, Onani mutuwo |