Genesis 28:18 - Buku Lopatulika18 Yakobo ndipo anauka m'mamawa, natenga mwala umene anaika pansi pamutu wake, nauimiritsa, nathira mafuta pamutu pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Yakobo ndipo anauka m'mamawa, natenga mwala umene anaika pansi pa mutu wake, nauimiritsa, nathira mafuta pamtu pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Yakobeyo adadzuka m'maŵa kwambiri, natenga mwala uja adaatsamirawu, nauimiritsa kuti ukhale mwala wachikumbutso. Tsono adauthira mafuta mwalawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Mmamawa mwake Yakobo anatenga mwala umene anatsamira mutu wake uja nawuyimika ngati chipilala ndi kuthira mafuta pamwamba pake Onani mutuwo |