Genesis 27:41 - Buku Lopatulika41 Ndipo Esau anamuda Yakobo chifukwa cha mdalitso umene atate wake anamdalitsa nao: ndipo Esau anati m'mtima mwake, Masiku a maliro a atate wanga ayandikira; pamenepo ndipo ndidzamupha mphwanga Yakobo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Ndipo Esau anamuda Yakobo chifukwa cha mdalitso umene atate wake anamdalitsa nao: ndipo Esau anati m'mtima mwake, Masiku a maliro a atate wanga ayandikira; pamenepo ndipo ndidzamupha mphwanga Yakobo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Motero Esau adadana naye Yakobe chifukwa choti m'malo modalitsa iyeyo, bambo wake adadalitsa Yakobe. Ndipo adati, “Nthaŵi yakuti ndilire maliro a bambo wanga ili pafupi, pamenepo ndidzamupha Yakobeyu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Ndipo Esau anamusungira chiwembu Yakobo chifukwa cha madalitso amene abambo ake anamupatsa. Esau anati kwa iye yekha, “Masiku olira abambo anga ayandikira; pambuyo pake ndidzamupha mʼbale wangayu Yakobo.” Onani mutuwo |