Genesis 24:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo anagwaditsa ngamira zake kunja kwa mzinda, ku chitsime cha madzi nthawi yamadzulo, nthawi yotuluka akazi kudzatunga madzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo anagwaditsa ngamira zake kunja kwa mudzi, ku chitsime cha madzi nthawi yamadzulo, nthawi yotuluka akazi kudzatunga madzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Atafika, adazigwaditsa pansi ngamirazo pafupi ndi chitsime, kunja kwa mzinda. Anali madzulo ndithu, nthaŵi imene akazi ankabwera kuchitsimeko kudzatunga madzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Atafika, anagwaditsa pansi ngamira zija pafupi ndi chitsime chimene chinali kunja kwa mzinda uja. Awa anali madzulo ndithu, nthawi imene amayi amapita kukatunga madzi. Onani mutuwo |