Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 21:34 - Buku Lopatulika

34 Ndipo Abrahamu anakhala ngati mlendo masiku ambiri m'dziko la Afilisti.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 Ndipo Abrahamu anakhala ngati mlendo masiku ambiri m'dziko la Afilisti.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Ndipo adakhala m'dziko la Afilisti nthaŵi yaitali.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Ndipo Abrahamu anakhala mʼdziko la Afilisti kwa nthawi yayitali.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 21:34
7 Mawu Ofanana  

Abrahamu ndipo anachoka kumeneko kunka ku dziko la kumwera, ndipo anakhala pakati pa Kadesi ndi Suri, ndipo anakhala ngati mlendo mu Gerari.


Ndipo Abrahamu anabwera kwa anyamata ake, ndipo anauka nayenda pamodzi kumuka ku Beereseba; ndipo anakhala Abrahamu pa Beereseba.


Pakuti ife ndife alendo pamaso panu, ndi ogonera, monga makolo athu onse; masiku athu a padziko akunga mthunzi, ndipo palibe kukhalitsa.


Imvani pemphero langa, Yehova, ndipo tcherani khutu kulira kwanga; musakhale chete pa misozi yanga; Pakuti ine ndine mlendo ndi Inu, wosakhazikika, monga makolo anga onse.


Iwo onse adamwalira m'chikhulupiriro, osalandira malonjezano, komatu adawaona ndi kuwalankhula kutali, navomereza kuti ali alendo ndi ogonera padziko.


Ndi chikhulupiriro anakhala mlendo kudziko la lonjezano, losati lake, nakhalira m'mahema pamodzi ndi Isaki ndi Yakobo, olowa nyumba pamodzi ndi iye a lonjezano lomwelo;


Okondedwa, ndikudandaulirani ngati alendo ndi ogonera mudzikanize zilakolako za thupi zimene zichita nkhondo pa moyo;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa