Genesis 21:34 - Buku Lopatulika34 Ndipo Abrahamu anakhala ngati mlendo masiku ambiri m'dziko la Afilisti. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Ndipo Abrahamu anakhala ngati mlendo masiku ambiri m'dziko la Afilisti. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Ndipo adakhala m'dziko la Afilisti nthaŵi yaitali. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Ndipo Abrahamu anakhala mʼdziko la Afilisti kwa nthawi yayitali. Onani mutuwo |